Letras Web

Malawi Native Anthem Text

Unknown

2 acessos

1.
Mlungu dalitsani Malawi,
Mumsunge m'mtendere.
Gonjetsani adani onse,
Njala, nthenda, nsanje.
Lunzitsani mitima yathu,
Kuti tisaope.
Mdalitse Mtsogo leri na fe,
Ndi Mai Malawi.
2.
Malawi ndziko lokongola,
La chonde ndi ufulu,
Nyanja ndi mphepo ya m'mapiri,
Ndithudi tadala.
Zigwa, mapiri, nthaka, dzinthu,
N'mphatso zaulere.
Nkhalango, madambo abwino.
Ngwokoma Malawi.
3.
O! Ufulu tigwirizane,
Kukweza Malawi.
Ndi chikondi, khama, kumvera,
Timutumikire.
Pa nkhondo nkana pa mtendere,
Cholinga n'chimodzi.
Mai, bambo, tidzipereke,
Pokweza Malawi.

Top Letras de Unknown

  1. Alma Mater Cornell
  2. Nauru Native Anthem Text
  3. Alpha Phi Omega Toast
  4. Malaysia Native Anthem Text
  5. Su Nombre Admirable!
  6. 99 Bottles Of Beer On The Wall
  7. Allison Gross
  8. Alberta
  9. South Africa Native Anthem Text
  10. Romania Native Anthem Text